Salimo 6:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Bwererani+ mudzapulumutse moyo wanga, inu Yehova.+Ndipulumutseni chifukwa cha kukoma mtima kwanu kosatha.+ Salimo 119:159 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 159 Onani kuti ndimakonda malamulo anu.+Inu Yehova, ndisungenibe wamoyo mwa kukoma mtima kwanu kosatha.+
4 Bwererani+ mudzapulumutse moyo wanga, inu Yehova.+Ndipulumutseni chifukwa cha kukoma mtima kwanu kosatha.+
159 Onani kuti ndimakonda malamulo anu.+Inu Yehova, ndisungenibe wamoyo mwa kukoma mtima kwanu kosatha.+