Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 Choncho anasankha Davide mtumiki wake,+

      Ndipo anamuchotsa kumakola a nkhosa.+

  • Yeremiya 45:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma iwe, ukufunafunabe zinthu zazikulu.+ Leka kuzifunafuna.”’+

      “‘Anthu onse ndikuwagwetsera tsoka+ ndipo iwe ndidzakupatsa moyo wako monga chofunkha chako kulikonse kumene ungapite,’ watero Yehova.”+

  • Amosi 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo Amosi anayankha Amaziya kuti: “Ine sindinali mneneri kapena mwana wa mneneri,+ koma ndinali m’busa+ ndiponso woboola nkhuyu.

  • Aroma 12:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Muziona ena mmene inuyo mumadzionera.+ Musamaganize modzikweza,+ koma khalani ndi mtima wodzichepetsa.+ Musadziyese anzeru.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena