Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuchokera kumwamba, Yehova wayang’ana,+

      Waona ana onse a anthu.+

  • Salimo 94:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova amadziwa kuti maganizo a anthu ali ngati mpweya wotuluka m’mphuno.+

  • Ezekieli 38:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Pa tsikulo maganizo adzakubwerera mumtima mwako+ ndipo udzaganiza zochita chiwembu choipa kwambiri.+

  • Mateyu 9:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma Yesu, podziwa zimene iwo anali kuganiza,+ ananena kuti: “N’chifukwa chiyani mukuganiza zinthu zoipa m’mitima mwanu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena