Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 145:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Yehova amachirikiza amene ali pafupi kugwa,+

      Ndipo amaweramutsa onse amene awerama chifukwa cha masautso.+

  • Salimo 147:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yehova amathandiza anthu ofatsa,+

      Koma anthu oipa amawagwetsera pansi.+

  • Luka 13:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo anaika manja ake pamayiyo, ndipo nthawi yomweyo anaweramuka,+ n’kuyamba kutamanda Mulungu.

  • 2 Akorinto 7:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Komabe Mulungu, amene amalimbikitsa+ osautsika mtima, anatilimbikitsa ndi kukhalapo* kwa Tito.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena