Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 37:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Khulupirira Yehova ndipo chita zabwino.+

      Khala padziko lapansi, ndipo khala wokhulupirika m’zochita zako zonse.+

  • Salimo 62:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Mukhulupirireni nthawi zonse, anthu inu.+

      Mukhuthulireni za mumtima mwanu.+

      Mulungu ndiye pothawirapo pathu.+ [Seʹlah.]

  • Miyambo 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Khulupirira Yehova ndi mtima wako wonse,+ ndipo usadalire luso lako lomvetsa zinthu.+

  • 1 Petulo 4:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho amene akuvutika mogwirizana ndi chifuniro cha Mulungu, aike miyoyo yawo m’manja mwa Mlengi wokhulupirika, pamene akupitiriza kuchita zabwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena