Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndithu ndikukuuzani, Kulikonse kumene uthenga wabwino udzalalikidwe m’dziko lonse,+ anthu azidzanenanso zimene mayiyu wachita kuti azidzam’kumbukira.”+

  • Machitidwe 9:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Pamenepo Petulo ananyamuka n’kupita nawo limodzi. Atafika kumeneko, iwo anamutengera m’chipinda cham’mwamba chija. Ndipo akazi onse amasiye anabwera kwa iye akulira ndi kumuonetsa malaya ambiri akunja ndi amkati+ amene Dorika anali kusoka pamene anali nawo.+

  • Aroma 16:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Mulandireni+ mwa Ambuye mmene mumalandirira oyerawo, ndi kumuthandiza pa nkhani iliyonse imene angafune thandizo lanu.+ Pakuti iyenso anateteza abale ambirimbiri, ngakhalenso ineyo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena