Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pakuti Yehova amadziwa njira za olungama,+

      Koma oipa adzatheratu pamodzi ndi njira zawo.+

  • Salimo 146:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova amayang’anira alendo okhala m’dziko la eni.+

      Amathandiza mwana wamasiye* ndi mkazi wamasiye.+

      Koma njira+ ya anthu oipa amaichititsa kukhala yovuta kuyendamo.+

  • Mateyu 7:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Lowani pachipata chopapatiza.+ Pakuti msewu waukulu ndi wotakasuka ukupita kuchiwonongeko, ndipo anthu ambiri akuyenda mmenemo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena