Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 23:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti iye amadziwa bwino njira imene ine ndimadutsa.+

      Akamaliza kundiyesa, ndidzakhala ngati golide.+

  • Salimo 37:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova amadziwa za moyo wa anthu osalakwa,+

      Ndipo cholowa chawo chidzakhalapo mpaka kalekale.+

  • Yeremiya 12:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Inu Yehova, mumandidziwa bwino.+ Mumandiona ndipo mumasanthula mtima wanga kuti muone ngati uli wokhulupirika kwa inu.+ Apatuleni ngati nkhosa zimene zikukaphedwa,+ ndipo aikeni padera kuyembekezera tsiku lokaphedwa.

  • 2 Timoteyo 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Komabe, maziko olimba a Mulungu adakali chikhalire,+ ndipo ali ndi chidindo cha mawu akuti: “Yehova* amadziwa anthu ake,”+ ndiponso akuti: “Aliyense wotchula dzina la Yehova+ aleke kuchita zosalungama.”+

  • 1 Petulo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti maso+ a Yehova* ali pa olungama, ndipo makutu ake amamva pembedzero lawo,+ koma nkhope ya Yehova imakwiyira anthu ochita zoipa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena