-
Ezekieli 27:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Ana aamuna a ku Arivadi+ pamodzi ndi gulu lako lankhondo anali kukhala pamwamba pa mpanda wako kuzungulira mzinda wonse. Pansanja zako panali amuna olimbikira nkhondo. Iwo anapachika zishango zawo zozungulira m’makoma ako kuzungulira mpandawo.+ Amuna amenewa anakuchititsa kuti ukhale chiphadzuwa.
-