Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 8:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Komanso Davide anatenga zishango zozungulira+ zagolide zimene zinali ndi atumiki a Hadadezeri ndipo anabwera nazo ku Yerusalemu.

  • 2 Mafumu 11:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano wansembeyo anapatsa atsogoleri a magulu a asilikali 100 aja mikondo ndi zishango zozungulira za Mfumu Davide, zomwe zinali m’nyumba ya Yehova.+

  • Ezekieli 27:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ana aamuna a ku Arivadi+ pamodzi ndi gulu lako lankhondo anali kukhala pamwamba pa mpanda wako kuzungulira mzinda wonse. Pansanja zako panali amuna olimbikira nkhondo. Iwo anapachika zishango zawo zozungulira m’makoma ako kuzungulira mpandawo.+ Amuna amenewa anakuchititsa kuti ukhale chiphadzuwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena