Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 23:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Koma anthu onse opanda pake+ amawakankhira kutali+ ngati zitsamba zaminga.+

      Pakuti zitsamba zamingazo sizigwiridwa ndi manja pozichotsa.

  • Yesaya 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kuwala kwa Isiraeli+ kudzasanduka moto+ ndipo Woyera wake adzasanduka lawi la moto.+ Iye adzayaka n’kunyeketsa udzu wake* ndi zitsamba zake zaminga+ pa tsiku limodzi.

  • Aheberi 6:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma ikatulutsa minga ndi mitula, imakanidwa ndipo imatsala pang’ono kutembereredwa.+ Mapeto ake imatenthedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena