Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 52:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Taona! Mtumiki wanga+ azidzachita zinthu mwanzeru.+ Iye adzakhala ndi udindo wapamwamba ndipo adzakwezedwa ndi kulemekezedwa kwambiri.+

  • Mateyu 12:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Taonani mtumiki wanga+ amene ndamusankha, wokondedwa wanga,+ amene moyo wanga ukukondwera naye. Ndidzaika mzimu wanga pa iye,+ ndipo adzasonyeza bwinobwino chilungamo chenicheni kwa anthu a mitundu ina.

  • Yohane 4:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Yesu anati: “Chakudya+ changa ndicho kuchita chifuniro+ cha amene anandituma ndi kutsiriza ntchito yake.+

  • Yohane 6:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Chifukwa ndinatsika kuchokera kumwamba+ kudzachita chifuniro cha iye amene anandituma, osati chifuniro changa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena