-
Ezekieli 9:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Kenako iye analankhula mokuwa ine ndikumva, kuti: “Uzani anthu amene asankhidwa kuti awononge mzindawu kuti abwere pafupi. Aliyense anyamule chida chake chowonongera.”
-