Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 7:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iwe uzimuuza zonse zimene ndizikulamula,+ koma Aroni m’bale wako azikulankhulira kwa Farao,+ ndipo adzaloladi ana a Isiraeli kuchoka m’dziko lake.+

  • Numeri 22:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Usikuwo Mulungu anafika kwa Balamu, n’kumuuza kuti: “Ngati anthuwa abwera kudzakuitana, nyamuka, pita nawo limodzi. Koma ukalankhule mawu okhawo amene ndikakuuze.”+

  • 2 Mbiri 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma Mikaya anati: “Pali Yehova Mulungu wamoyo,+ zimene Mulungu wanga anene n’zimene ndikalankhule.”+

  • Yeremiya 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Imvani mawu a pangano langa, anthu inu!

      “Anthu a ku Yuda komanso okhala mu Yerusalemu ukawauze+ mawu amenewa.

  • Ezekieli 3:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Iye anapitiriza kundiuza kuti: “Iwe mwana wa munthu, pita pakati pa nyumba+ ya Isiraeli ndipo ukawauze mawu anga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena