Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno Yehu anatuluka n’kupita kwa atumiki a mbuye wake. Atumikiwo anayamba kum’funsa kuti: “Zili bwino kodi?+ Nanga munthu wamisalayu+ amadzatani kwa iwe?” Koma iye anawayankha kuti: “Inuyo mukum’dziwa bwino munthuyu ndiponso zonena zake.”

  • Hoseya 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Masiku oti uyenderedwe adzafika,+ masiku oti ulipire adzakwana+ ndipo anthu a Isiraeli adzadziwa zimenezi.+ Mneneri adzapusa+ ndipo munthu wolankhula mawu ouziridwa adzalusa, chifukwa cha kuchuluka kwa zolakwa zako+ ndiponso chifukwa cha kuchuluka kwa chidani.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena