Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 40:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Patapita nthawi, akuluakulu onse a magulu ankhondo amene anali m’madera a kunja kwa mzinda+ pamodzi ndi anthu awo, anamva kuti mfumu ya Babulo yaika Gedaliya mwana wa Ahikamu kukhala wolamulira dzikolo. Anamvanso kuti yamuika kuti azilamulira amuna, akazi, ana ndi anthu onyozeka m’dzikolo amene sanatengedwe kupita ku ukapolo ku Babulo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena