Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kodi nkhwangwa ingadzikuze kuposa munthu amene akuigwiritsa ntchito? Kapena kodi chochekera matabwa chingadzikweze kuposa munthu amene akuchigwiritsa ntchito? Kodi chikwapu chinganyamule munthu amene wachinyamula m’mwamba, ndiponso kodi ndodo inganyamule m’mwamba munthu amene si mtengo?+

  • Yesaya 14:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 amene anali kumenya mwaukali anthu a mitundu yosiyanasiyana powakwapula mosalekeza,+ ndiponso amene anali kugonjetsa mitundu ya anthu mokwiya, ndi chizunzo chopanda malire.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena