20 Tsopano amuna inu, tamverani zimene Yehova wasankha kuchitira Edomu+ ndiponso zimene waganiza kuti achitire anthu okhala ku Temani:+ Ndithudi, chilombo chidzakokera ana a nkhosa uku ndi uku, ndipo chidzawononga malo awo okhala chifukwa cha anthuwo.+