-
Ezekieli 34:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 “‘Choncho Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kwa iwo kuti: “Ndithu ine ndidzapereka chiweruzo pakati pa nkhosa yonenepa ndi nkhosa yowonda.
-