Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 12:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Anthu a m’dzikoli uwauze kuti, ‘Izi n’zimene Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kwa anthu okhala mu Yerusalemu, okhala m’dziko la Isiraeli:+ “Adzadya chakudya ndi nkhawa ndipo adzamwa madzi ndi mantha, pakuti dzikolo lidzakhala bwinja.+ Zinthu zonse za mmenemo zidzachotsedwa chifukwa cha zinthu zachiwawa zimene anthu onse okhala mmenemo akuchita.+

  • Ezekieli 20:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 “‘Ndikadzakulowetsani m’dziko la Isiraeli,+ dziko limene ndinalumbira nditakweza dzanja kuti ndidzalipereka kwa makolo anu, anthu inu mudzadziwa kuti ine ndine Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena