2 Mbiri 36:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kuwonjezera pamenepo, Zedekiya anapandukira Mfumu Nebukadinezara+ yomwe inali itamulumbiritsa kwa Mulungu,+ ndipo anapitiriza kuumitsa khosi lake ndi mtima wake+ kuti asabwerere kwa Yehova Mulungu wa Isiraeli. Ezekieli 17:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kuwonjezera apo, inatenga mmodzi wa mbewu yachifumu+ n’kuchita naye pangano ndi kumulumbiritsa.+ Mfumuyo inatenga atsogoleri a m’dzikolo n’kupita nawo kwawo,+
13 Kuwonjezera pamenepo, Zedekiya anapandukira Mfumu Nebukadinezara+ yomwe inali itamulumbiritsa kwa Mulungu,+ ndipo anapitiriza kuumitsa khosi lake ndi mtima wake+ kuti asabwerere kwa Yehova Mulungu wa Isiraeli.
13 Kuwonjezera apo, inatenga mmodzi wa mbewu yachifumu+ n’kuchita naye pangano ndi kumulumbiritsa.+ Mfumuyo inatenga atsogoleri a m’dzikolo n’kupita nawo kwawo,+