Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 26:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wauza mzinda wa Turo kuti, ‘Kodi zilumba sizidzagwedezeka chifukwa cha phokoso la kuwonongedwa kwako, kubuula kwa anthu ovulazidwa koopsa, ndi kuphedwa kwa anthu ako ambiri?+

  • Chivumbulutso 18:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Zachisoni, chifukwa mu ola limodzi, chuma chochulukachi chawonongedwa!’+

      “Woyendetsa ngalawa aliyense ndi munthu aliyense woyenda panyanja kuchokera kulikonse,+ ogwira ntchito m’ngalawa ndi onse oyenda panyanja pochita malonda awo, anaima patali.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena