17 Zachisoni, chifukwa mu ola limodzi, chuma chochulukachi chawonongedwa!’+
“Woyendetsa ngalawa aliyense ndi munthu aliyense woyenda panyanja kuchokera kulikonse,+ ogwira ntchito m’ngalawa ndi onse oyenda panyanja pochita malonda awo, anaima patali.+