Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 31:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Udzabzala mpesa kumapiri a ku Samariya.+ Obzala mpesawo adzadya zipatso zake.+

  • Ezekieli 36:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Anthu a mitundu ina okuzungulirani amene adzatsale, adzadziwa kuti ine Yehova, ndamanga zinthu zimene zinagwetsedwa.+ Adzadziwa kuti ndabzala mitengo m’dziko limene linali bwinja. Ine Yehova ndanena zimenezi ndipo ndazichita.’+

  • Amosi 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo ndidzasonkhanitsa ndi kubwezeretsa anthu anga Aisiraeli amene anagwidwa ndi kutengedwa kupita ku ukapolo.+ Iwo adzamanga mizinda imene ili yabwinja ndi kukhalamo.+ Adzalima minda ya mpesa ndi kumwa vinyo wochokera m’mindayo. Adzalimanso minda ya zipatso ndi kudya zipatso zochokera m’mindayo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena