Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 63:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Koma ofuna kuwononga moyo wanga,+

      Adzatsikira kumanda.+

  • Ezekieli 31:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho sipadzakhalanso mtengo uliwonse wothiriridwa bwino umene udzakhale wautali kwambiri kapena umene nsonga zake zidzafike m’mitambo. Sipadzakhala mtengo uliwonse umene uli pamadzi ambiri umene udzatalike kukafika m’mitambo, pakuti mitengo yonse idzakhala itadulidwa.+ Yonse idzakhala itatsikira pansi pa nthaka+ pamodzi ndi ana a anthu amene akutsikira kudzenje.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena