Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Wakhala ngati mbidzi+ yaikazi yozolowera kukhala m’chipululu imene ili ndi chilakolako champhamvu, imene ikupuma mwawefuwefu.+ Ndani angaibweze pa nthawi yake yokweredwa? Mbidzi zamphongo zoifunafuna sizidzavutika kuipeza. M’mwezi wake wokweredwa zidzaipeza.

  • Ezekieli 23:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Choncho ndinam’pereka m’manja mwa amuna amene anali kukhumba kugona naye.+ Ndinam’pereka m’manja mwa ana aamuna a ku Asuri amene iye anali kuwakhumba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena