-
Danieli 4:25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
25 Inuyo adzakuthamangitsani pakati pa anthu ndipo muzidzakhala pakati pa nyama zakutchire.+ Muzidzadya udzu ngati ng’ombe+ ndipo muzidzanyowa ndi mame akumwamba. Ndiyeno padzadutsa nthawi zokwanira 7+ kufikira mutadziwa kuti Wam’mwambamwamba ndiye Wolamulira wa maufumu a anthu,+ ndiponso kuti akafuna kupereka ulamuliro kwa munthu aliyense, amamupatsa.+
-
-
Danieli 4:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 ndipo akuthamangitsa pakati pa anthu. Uyamba kukhala pakati pa nyama zakutchire+ ndipo uzidzadya udzu ngati ng’ombe. Ndiyeno padutsa nthawi zokwanira 7 kufikira utadziwa kuti Wam’mwambamwamba ndiye Wolamulira wa maufumu a anthu, ndiponso kuti akafuna kupereka ulamuliro kwa munthu aliyense, amamupatsa.’”+
-