-
Danieli 5:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Anachita zimenezi chifukwa munthuyu anali ndi luso lodabwitsa, anali wodziwa zinthu ndi wozindikira pa nkhani yomasulira maloto,+ kumasulira mikuluwiko ndi kumasula mfundo. Zinthu zonsezi zinapezeka mwa munthu ameneyu+ Danieli, amene mfumu inamupatsa dzina lakuti Belitesazara.+ Tsopano itanani Danieli kuti adzakuuzeni kumasulira kwa zolembedwazi.”
-