-
Ezekieli 43:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Sadzaipitsanso dzina langa poika khomo lawo pafupi ndi khomo langa. Sadzaikanso felemu la khomo lawo pafupi ndi felemu la khomo langa moti pakati pa iwowo ndi ine n’kungokhala khoma lokha lotisiyanitsa.+ Iwo anaipitsa dzina langa loyera ndi zinthu zawo zonyansa zimene anali kuchita+ moti ndinawafafaniza nditakwiya.+
-