Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 9:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tsopano munthu wovala zovala zansalu uja, yemwe m’chiuno mwake munali kachikwama konyamuliramo inki ndi zolembera, anabwera n’kudzanena kuti: “Ndachita monga momwe munanditumira.”+

  • Yona 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Koma ine, ndidzakutamandani ndi kupereka nsembe kwa inu.+

      Zimene ndalonjeza ndidzazikwaniritsa.+ Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena