Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Titangomva zimenezi, mitima yathu inayamba kusungunuka ndi mantha,+ ndipo mpaka pano palibe aliyense amene akulimba mtima, chifukwa choopa inu.+ Ndithu, Yehova Mulungu wanu ndiye Mulungu wa kumwamba ndi padziko lapansi.+

  • Salimo 22:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndathiridwa pansi ngati madzi.+

      Mafupa anga onse alekanalekana.+

      Mtima wanga wakhala ngati phula,+

      Wasungunuka mkati mwanga.+

  • Yesaya 13:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 N’chifukwa chake anthu onse adzataya mtima, ndipo mitima ya anthu onse idzasungunuka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena