Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mneneri Hagai+ ndi mneneri Zekariya+ mdzukulu wa Ido,+ analosera kwa Ayuda amene anali mu Yuda ndi mu Yerusalemu, m’dzina+ la Mulungu wa Isiraeli yemwe anali nawo.+

  • Zekariya 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pa tsiku la 24, m’mwezi wa 11 womwe ndi mwezi wa Sebati, m’chaka chachiwiri cha ulamuliro wa Dariyo,+ Yehova anaonetsa masomphenya mneneri Zekariya,+ mwana wa Berekiya, mwana wa Ido.+ Masomphenya amene ndinaonawo ndi awa:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena