Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 33:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndipo anati:

      “Yehova anafika kuchokera ku Sinai,+

      Anathwanima pa iwo kuchokera ku Seiri.+

      Anawala kuchokera kudera lamapiri la Parana,+

      Ndipo anali ndi miyandamiyanda ya oyera ake,+

      Kudzanja lake lamanja kunali ankhondo ake.+

  • Salimo 149:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kuti awaweruze motsatira chigamulo cholembedwa.+

      Ulemerero umenewu ndi wa anthu onse okhulupirika a Mulungu.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Yoweli 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu mitundu ya anthu yokhala mozungulira, bwerani mudzathandizane+ ndipo nonse musonkhane pamodzi.’”+

      Inu Yehova, bweretsani ankhondo anu kumalo amenewo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena