Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 1:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma Yesu anadzudzula mzimuwo kuti: “Khala chete, ndipo tuluka mwa iye!”+

  • Luka 9:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Koma ngakhale pamene anali kufika naye kwa iye, chiwandacho chinamugwetsa pansi ndi kum’tsalimitsa mwamphamvu. Yesu anakalipira mzimu wonyansawo ndi kuchiritsa mnyamatayo. Kenako anamupereka kwa bambo ake.+

  • Yuda 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma pamene Mikayeli+ mkulu wa angelo+ anasemphana maganizo+ ndi Mdyerekezi ndipo anakangana naye za mtembo wa Mose,+ sanayese n’komwe kumuweruza ndi mawu onyoza,+ m’malomwake anati: “Yehova akudzudzule.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena