21 Ndiyeno kapolo uja anabwerera kukanena zimenezi kwa mbuye wake. Pamenepo mwininyumba anakwiya ndi kuuza kapolo wake kuti, ‘Pita mwamsanga m’misewu ndi m’njira za mumzindawu, ukatenge anthu osauka, otsimphina, akhungu ndi olumala ndi kubwera nawo kuno.’+