Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 27:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho mukawoloka Yorodano, muimike miyala imeneyi paphiri la Ebala,+ monga mmene ndakulamulirani lero, ndipo muipake utoto woyera.+

  • Luka 11:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Tsoka inu, chifukwa muli ngati manda achikumbutso osaonekera, moti anthu amayenda pamwamba pake koma osadziwa!”+

  • Machitidwe 23:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pamenepo Paulo anamuuza kuti: “Uona, Mulungu akukantha, khoma* lopaka laimu+ iwe. Wakhala pamenepo kuti undiweruze motsatira Chilamulo,+ kodi ukuphwanyanso wekha Chilamulocho+ polamula kuti andimenye?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena