Luka 11:44 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 44 Tsoka kwa inu, chifukwa muli ngati manda* amene sakuoneka bwinobwino*+ moti anthu amayenda pamwamba pake koma osadziwa!” Luka Buku Lofufuzira Nkhani la Mboni za Yehova la 2019 11:44 Yesu—Ndi Njira, tsa. 178 Nsanja ya Olonda,9/1/1988, tsa. 24
44 Tsoka kwa inu, chifukwa muli ngati manda* amene sakuoneka bwinobwino*+ moti anthu amayenda pamwamba pake koma osadziwa!”