7 Komanso, mukadzamva phokoso la nkhondo ndi mbiri za nkhondo, musadzachite mantha. Zimenezi ziyenera kuchitika ndithu, koma mapeto adzakhala asanafikebe.+
9 Komanso, mukadzamva phokoso la nkhondo ndi zipolowe, musadzachite mantha.+ Pakuti zimenezi ziyenera kuchitika choyamba, koma mapeto sadzafika nthawi yomweyo.”