Ekisodo 21:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Ngati yagunda kapolo wamwamuna kapena wamkazi, mwiniwake azilipira ndalama zokwana masekeli* 30+ kwa mbuye wa kapoloyo, ndipo ng’ombeyo iziponyedwa miyala. Zekariya 11:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Kenako ndinawauza kuti: “Ngati mukuona kuti n’zoyenera,+ ndipatseni malipiro anga, koma ngati mukuona kuti n’zosayenera musandipatse.” Pamenepo iwo anandipatsa ndalama 30 zasiliva monga malipiro anga.+ Mateyu 27:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pamenepo Yudasi amene anam’pereka uja ataona kuti Yesu waweruzidwa kuti aphedwe, anavutika koopsa mumtima mwake moti anapita kukabweza ndalama 30+ zasiliva zija kwa ansembe aakulu ndiponso akulu. Maliko 14:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Atamva zimenezo, iwo anasangalala ndi kumulonjeza kuti am’patsa ndalama zasiliva.+ Choncho iye anayamba kufunafuna mpata wabwino umene angamuperekere.+ Luka 22:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Iwo anakondwa, ndipo anagwirizana kuti amupatse ndalama zasiliva.+
32 Ngati yagunda kapolo wamwamuna kapena wamkazi, mwiniwake azilipira ndalama zokwana masekeli* 30+ kwa mbuye wa kapoloyo, ndipo ng’ombeyo iziponyedwa miyala.
12 Kenako ndinawauza kuti: “Ngati mukuona kuti n’zoyenera,+ ndipatseni malipiro anga, koma ngati mukuona kuti n’zosayenera musandipatse.” Pamenepo iwo anandipatsa ndalama 30 zasiliva monga malipiro anga.+
3 Pamenepo Yudasi amene anam’pereka uja ataona kuti Yesu waweruzidwa kuti aphedwe, anavutika koopsa mumtima mwake moti anapita kukabweza ndalama 30+ zasiliva zija kwa ansembe aakulu ndiponso akulu.
11 Atamva zimenezo, iwo anasangalala ndi kumulonjeza kuti am’patsa ndalama zasiliva.+ Choncho iye anayamba kufunafuna mpata wabwino umene angamuperekere.+