Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Zoona, Mwana wa munthu akuchokadi, monga Malemba amanenera za iye. Koma tsoka kwa munthu amene akupereka Mwana wa munthu! Zikanakhala bwino munthu ameneyu akanapanda kubadwa.”+

  • Yohane 17:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pamene ndinali nawo pamodzi, ndinali kuwayang’anira+ chifukwa cha dzina lanu limene mwandipatsa. Ine ndawasunga moti palibe aliyense wa iwo amene wawonongeka+ kupatulapo mwana wa chiwonongeko,+ kuti malemba akwaniritsidwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena