Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 16:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsopano iwo atatuluka, m’manda achikumbutsowo anayamba kuthawa, pakuti anali kunjenjemera ndi kunthunthumira kwambiri. Ndipo sanaulule kanthu kwa aliyense, chifukwa anagwidwa ndi mantha.+

      MAWU OMALIZA AAFUPI

      Mipukutu ndi Mabaibulo ena amene analembedwa pambuyo pake ali ndi mawu omaliza aafupi awa pambuyo pa Maliko 16:8:

      Koma zinthu zonse zimene analamula, iwo anazifotokoza mwachidule kwa amene anali pafupi ndi Petulo. Komanso izi zitatha, Yesu mwiniyo anatumiza uthenga woyera ndi wosawonongeka wa chipulumutso chosatha kudzera mwa ophunzira, kuchokera kum’mawa mpaka kumadzulo.

  • Luka 24:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepo anachoka kumanda achikumbutsowo n’kubwerera kukanena zonsezi kwa ophunzira 11 aja ndi kwa ena onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena