Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aefeso 4:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Kwiyani, koma musachimwe.+ Dzuwa lisalowe muli chikwiyire,+

  • Akolose 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma tsopano zonsezo muzitaye kutali ndi inu.+ Mutaye mkwiyo, kupsa mtima, kuipa, ndi mawu achipongwe,+ ndipo pakamwa panu pasatuluke nkhani zotukwana.+

  • Yakobo 1:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Abale anga okondedwa, dziwani izi: Munthu aliyense akhale wofulumira kumva, wodekha polankhula,+ wosafulumira kukwiya,+

  • Yakobo 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Mwaweruza ndi kupha munthu wolungama. Iye akukutsutsani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena