Maliko 4:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Pakuti chilichonse chobisidwa chidzaululika. Chilichonse chimene chimasungidwa mwachinsinsi kwambiri chidzadziwika.+ Luka 8:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Chilichonse chobisidwa+ chidzaonekera poyera. Ndipo zinthu zonse zosungidwa mwachinsinsi kwambiri zidzadziwika ndi kuululika.+ 1 Akorinto 4:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Chotero musaweruze+ kalikonse nthawi isanakwane, mpaka Ambuye adzafike.+ Akadzafika adzaunika zinsinsi za mu mdima+ ndi kuonetsa poyera+ zolingalira za m’mitima, ndipo aliyense adzatamandidwa yekha ndi Mulungu.+
22 Pakuti chilichonse chobisidwa chidzaululika. Chilichonse chimene chimasungidwa mwachinsinsi kwambiri chidzadziwika.+
17 Chilichonse chobisidwa+ chidzaonekera poyera. Ndipo zinthu zonse zosungidwa mwachinsinsi kwambiri zidzadziwika ndi kuululika.+
5 Chotero musaweruze+ kalikonse nthawi isanakwane, mpaka Ambuye adzafike.+ Akadzafika adzaunika zinsinsi za mu mdima+ ndi kuonetsa poyera+ zolingalira za m’mitima, ndipo aliyense adzatamandidwa yekha ndi Mulungu.+