Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 24:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Komanso, pa nthawiyo anthu ambiri adzapunthwa+ ndipo adzaperekana ndi kudana.+

  • Maliko 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Amakhala opanda mizu mwa iwo okha, ndipo amapitirizabe kwakanthawi. Koma chisautso kapena mazunzo akangobuka chifukwa cha mawuwo, iwo amapunthwa.+

  • Luka 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zogwera pathanthwe ndi anthu amene amati akangomva mawuwo, amawalandira ndi chimwemwe, koma oterewa alibe mizu. Amakhulupirira kwa kanthawi, koma nthawi yoyesedwa ikafika amagwa.+

  • 2 Timoteyo 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Iwe ukudziwa kuti anthu onse m’chigawo cha Asia+ andisiya.+ Ena mwa iwo ndi Fugelo ndi Heremogene.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena