Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 6:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Ndipo onse amene anadya mkatewo anali amuna okwana 5,000.+

  • Luka 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pamenepo panali amuna pafupifupi 5,000.+ Koma Yesu anauza ophunzira ake kuti: “Auzeni akhale m’magulu, muja amakhalira akamadya chakudya. Pagulu lililonse pakhale anthu pafupifupi 50.”+

  • Yohane 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yesu ananena kuti: “Akhazikeni pansi anthuwa muja amakhalira pa chakudya.”+ Pamalopo panali udzu wambiri. Choncho amuna pafupifupi 5,000 anakhaladi pansi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena