Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 13:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kenako atauza khamu la anthulo kuti lizipita, analowa m’nyumba. Ndipo ophunzira ake anabwera kwa iye ndi kunena kuti: “Timasulireni fanizo lija la namsongole m’munda.”

  • Maliko 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano pamene anakhala payekha, ena amene anali naye chapafupi limodzi ndi atumwi 12 aja, anayamba kum’funsa za mafanizo aja.+

  • Luka 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Koma ophunzira ake anayamba kumufunsa tanthauzo la fanizo limeneli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena