Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 7:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Tsopano ndikunena kwa osakwatira+ ndi kwa akazi amasiye kuti, ndi bwino akhalebe mmene ineyo ndililimu.+

  • 1 Akorinto 7:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Nayenso amene walekana ndi moyo wokhala yekha* n’kulowa m’banja wachita bwino,+ koma amene sanalowe m’banja wachita bwino koposa.+

  • 1 Akorinto 7:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Komabe angakhale wosangalala kwambiri ngati apitiriza mmene alili.+ Ndi mmene ine ndikuonera. Ndipo ndine wotsimikiza mtima kuti ndilinso ndi mzimu wa Mulungu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena