Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 8:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Chotero amunawo anadabwa n’kunena kuti: “Kodi munthu ameneyu ndi wotani,+ moti ngakhale mphepo ndi nyanja zikum’mvera?”

  • Luka 8:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Ndiyeno anawafunsa kuti: “Chikhulupiriro chanu chili kuti?” Koma iwo anagwidwa ndi mantha ndipo anathedwa nzeru, mwakuti anayamba kufunsana kuti: “Kodi ameneyu ndani kwenikweni, wochita kulamula mphepo ndi madzi ndipo n’kumumvera?”+

  • Yohane 6:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma atapalasa makilomita pafupifupi 5 kapena 6, anaona Yesu akuyenda panyanja, kuyandikira ngalawayo ndipo iwo anachita mantha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena