Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 9:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Koma ophunzirawo sanamvetsebe tanthauzo la mawu amenewa. Tanthauzo lake linabisika kwa iwo kuti asazindikire, ndipo anaopa kumufunsa za mawu amenewa.+

  • Yohane 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yesu anadziwa+ kuti akufuna kumufunsa, choncho iye anawafunsa kuti: “Kodi mukufunsana nokhanokha zimenezi, chifukwa ndanena kuti, Kwa kanthawi simudzandiona, ndipo kwa kanthawi mudzandiona?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena