Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 21:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kenako Yesu analowa m’kachisi ndi kuthamangitsa onse ogulitsa ndi ogula m’kachisimo, ndipo anagubuduza matebulo a osintha ndalama ndi mabenchi a ogulitsa nkhunda.+

  • Luka 19:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Ndiyeno analowa m’kachisi n’kuyamba kuthamangitsa anthu amene anali kugulitsamo zinthu,+

  • Yohane 2:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kumeneko anapeza ogulitsa ng’ombe, nkhosa ndi nkhunda+ komanso osintha ndalama ali m’kachisi atakhala m’mipando yawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena