Mateyu 9:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Mwachitsanzo, chapafupi n’chiti, kunena kuti, Machimo ako akhululukidwa, kapena kunena kuti, Nyamuka uyende?+ Luka 5:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Chapafupi n’chiti, kunena kuti, ‘Machimo ako akhululukidwa,’ kapena kunena kuti, ‘Nyamuka uyende’?+
5 Mwachitsanzo, chapafupi n’chiti, kunena kuti, Machimo ako akhululukidwa, kapena kunena kuti, Nyamuka uyende?+
23 Chapafupi n’chiti, kunena kuti, ‘Machimo ako akhululukidwa,’ kapena kunena kuti, ‘Nyamuka uyende’?+