Mateyu 26:65 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 65 Pamenepo mkulu wa ansembe anang’amba malaya ake akunja n’kunena kuti: “Wanyoza Mulungu!+ Nanga n’kufunanso mboni zina pamenepa?+ Pano mwadzimvera nokha mmene akunyozera Mulungu.+ Maliko 14:63 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 63 Tsopano mkulu wa ansembe atamva zimenezi anang’amba malaya ake amkati+ ndi kunena kuti: “Nanga n’kufunanso mboni zina pamenepa?+
65 Pamenepo mkulu wa ansembe anang’amba malaya ake akunja n’kunena kuti: “Wanyoza Mulungu!+ Nanga n’kufunanso mboni zina pamenepa?+ Pano mwadzimvera nokha mmene akunyozera Mulungu.+
63 Tsopano mkulu wa ansembe atamva zimenezi anang’amba malaya ake amkati+ ndi kunena kuti: “Nanga n’kufunanso mboni zina pamenepa?+